Mawu a M'munsi
a Bukuli linanenso kuti: “Anthu onse olemba mbiri yokhudza Chikhristu amene anakhala ndi moyo Constantine asanayambe kulamulira ufumu wa Roma [306-337 C.E.] ankadana ndi nkhondo.” Koma zinthu zinasintha anthu ampatuko atachuluka, monga mmene Baibulo linaloserera.—Machitidwe 20:29, 30; 1 Timoteyo 4:1.