Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Ngati ndinu a Mboni za Yehova ndipo mkazi wanu watsala pang’ono kuchira, mungachite bwino kudziwitsa Komiti Yolankhulana ndi Achipatala (HLC) ya kudera kwanu. Anthu a m’komiti imeneyi amayenda m’zipatala kuti athandize madokotala kusamalira odwala a Mboni popanda kugwiritsa ntchito magazi. Komanso anthu a m’komiti imeneyi angathandize kupeza dokotala amene amalemekeza zimene wodwala amakhulupirira komanso amene amadziwa bwino kuthandiza anthu popanda kugwiritsa ntchito magazi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena