Mawu a M'munsi
a Nyuzipepala ina kumeneko inanena kuti: “Panthawi imene mphepo yamkuntho imagwetsa nyumba, Mboni za Yehova zinali zotanganidwa kumanga tchalitchi chawo [Nyumba ya Ufumu]. Panali anthu ambiri ongodzipereka ndipo anamaliza ntchitoyi m’masiku atatu okha.”—Gibraltar Chronicle.