Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Posachedwapa, ofufuza apeza kuti molekyu ya RNA ndi yofunika kwambiri. Ngati RNA siikugwira bwino ntchito, munthu amatha kupezeka ndi matenda monga khansa, matenda enaake a pakhungu (psoriasis) ngakhalenso matenda oopsa kwambiri a mu ubongo (Alzheimer’s). Zimenezi zikusonyeza kuti mbali imeneyi, yomwe poyamba inkaoneka kuti ndi yopanda ntchito, ingathandize madokotala kudziwa matenda amene munthu akudwala komanso kuchiza matendawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena