Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zikuoneka kuti maganizo amenewa anawayambitsa ndi bishopu Isidore wa ku Seville, ku Spain (yemwe anabadwa mu 560 n’kumwalira mu 636 C.E.). Bishopuyu ananena kuti: “Pali zilankhulo zitatu zopatulika izi: Chiheberi, Chigiriki, ndi Chilatini. Ndipo zilankhulo zimenezi n’zapamwamba kuposa zilankhulo zonse padzikoli, chifukwa mlandu wa Ambuye unalembedwa pamtanda ndi Pilato m’zilankhulo zitatu zimenezi.” Koma mfundo imeneyi si yomveka chifukwa si Mulungu amene analamula kuti mlanduwo ulembedwe m’zilankhulo zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena