Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a James anabadwa m’chaka cha 1566 ndipo anasankhidwa kukhala Mfumu James yanambala 6 ya ku Scotland m’chaka chotsatira. M’chaka cha 1603 anasankhidwa kukhala Mfumu James Yoyamba ya ku England ndipo anayamba kulamulira mayiko onse awiri. Ndipo m’chaka cha 1604, mfumuyi inayamba kudziwika ndi dzina lakuti “Mfumu James ya ku Britain.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena