Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Werengani 1 Mbiri 1:27-34; 2:1-15; 3:1-24. Pamene Rehobowamu, yemwe anali mwana wa Mfumu Solomo, ankalamulira, mtundu wa Isiraeli unagawanika n’kukhala maufumu awiri, wina unali kumpoto ndipo wina unali kum’mwera. Kuyambira nthawi imeneyo, mtundu wa Isiraeli unkalamuliridwa ndi mafumu awiri pa nthawi imodzi.—1 Mafumu 12:1-24.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena