Mawu a M'munsi
c Mawu akuti “wanga” mu ulosi umenewu akunena za Khristu. Mwachitsanzo vesi 8 limanena kuti: “Amene [Mulungu] adzanene kuti ndine [Yesu Khristu] wolungama ali pafupi.” Yesu ali padziko lapansi anali munthu yekhayo amene Mulungu ankamuona kuti anali wolungama kapena kuti wopanda uchimo.—Aroma 3:23; 1 Petulo 2:21, 22.