Mawu a M'munsi
d Lemba la Yesaya 52:13-15 ndi la Yesaya 53:1-12 lili ndi maulosi ena onena za Mesiya. Mwachitsanzo, pa Yesaya 53:7 pamati: “Anatengedwa ngati nkhosa yopita kokaphedwa . . . sanatsegule pakamwa pake.” Ndipo vesi 10 limanena kuti anapereka moyo wake “monga nsembe ya kupalamula.”