Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

e Palinso anthu ena olemba mabuku akale omwe amanena za Khristu. Ena mwa anthuwa ndi Sutoniyasi, (anakhala m’nthawi ya atumwi), Pliny Wamng’ono yemwe anali bwanamkubwa wa ku Bituniya (anakhala ndi moyo chakumayambiriro kwa 100 C.E) ndi wolemba mbiri yakale dzina lake Josephus, (anakhala m’nthawi ya atumwi) yemwe ananena za “Yakobo, m’bale wake wa Yesu yemwe ankatchedwanso Khristu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena