Mawu a M'munsi
e Palinso anthu ena olemba mabuku akale omwe amanena za Khristu. Ena mwa anthuwa ndi Sutoniyasi, (anakhala m’nthawi ya atumwi), Pliny Wamng’ono yemwe anali bwanamkubwa wa ku Bituniya (anakhala ndi moyo chakumayambiriro kwa 100 C.E) ndi wolemba mbiri yakale dzina lake Josephus, (anakhala m’nthawi ya atumwi) yemwe ananena za “Yakobo, m’bale wake wa Yesu yemwe ankatchedwanso Khristu.”