Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Priestley asanatulukire mpweya wa okosijeni, katswiri wina wofufuza mmene zinthu zimapangidwira wa ku Sweden, dzina lake Carl Scheele anatulukirapo mpweyawu koma sanalembe zimene anatulukirazi. Patapita nthawi kuchokera pamene Priestley anatulukira mpweyawu, katswiri winanso wofufuza mmene zinthu zimapangidwira wa ku France, dzina lake Antoine-Laurent Lavoisier, anatchula mpweyawu kuti okosijeni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena