Mawu a M'munsi
a Kuti mudziwe za cholinga cha Mulungu chokhudza dziko lapansili, werengani mutu 3 m’buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova. Bukuli likupezekanso pa webusaiti yathu ya www.pr418.com/ny.