Mawu a M'munsi
a Anthu a ku Spain ankagwiritsa ntchito mawu akuti a Morisco monyoza, ponena za Asilamu omwe anayamba Chikatolika. Ufumu womaliza wachisilamu utagonjetsedwa mu 1492, anthuwa anayamba kukhala pachilumba cha Iberia. Akatswiri a mbiri yakale akamanena za anthuwa amagwiritsanso ntchito mawu omwewa, koma osati monyoza.