Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Akatswiri a sayansi ya zinthu zakuthambo a ku Greece ndi amene anali oyamba kuchita zimenezi. Akatswiri a maphunziro achisilamu ankagwiritsa ntchito njirayi pofuna kudziwa kumene kuli mzinda wa Mecca womwe ndi wofunika kwambiri m’chipembedzo chachisilamu. Masiku anonso, Asilamu amayang’ana komwe kuli mzinda wa Mecca akamapemphera ndiponso akamazinga nyama. Komanso akamaika maliro, amawayang’anitsa komwe kuli mzindawu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena