Mawu a M'munsi
a Kuti mudziwe zambiri pa nkhani yonena za Babulo Wamkulu, zomwe zimachitika munthu akamwalira, kukhulupirira mizimu komanso nkhani zina, werengani buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? Bukuli likupezekanso pa webusaiti yathu ya www.jw.org/ny.