Mawu a M'munsi
a Kuti mudziwe mfundo zina zomwe zingathandize kuti banja lanu lizikhala losangalala, werengani mutu 14 m’buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? Bukuli ndi lofalitsidwa ndi a Mboni za Yehova ndipo likupezeka pa webusaiti ya www.pr418.com/ny. Pa webusaitiyi palinso nkhani zina zothandiza mabanja. Pitani pamene palembedwa kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MALANGIZO OTHANDIZA BANJA LONSE.