Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Si bwino kuchotsa mimba chifukwa choti dokotala wakuuzani kuti moyo wa mayi kapena wa mwana ukhoza kukhala pa ngozi. Koma ngati pa nthawi yobereka mayi ndi bambo auzidwa kuti ayenera kusankha pakati pa kupulumutsa moyo wa mayi kapena wa mwana, iwo ayenera kusankha okha zochita. Komabe masiku ano zimenezi sizichitikachitika m’mayiko ena chifukwa choti zipatala zawo zili ndi zipangizo zamakono.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena