Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Komabe, iye safunikira chophimba kumutu, pamene alalikira kunyumba ndi nyumba, chifukwa chakuti thayo la kulalikira mbiri yabwino liri la Akristu onse. Koma ngati mikhalidwe imafunikiritsa kuti achititse phunziro la Baibulo la panyumba pamene mwamuna wake alipo (mutu wake, ngakhale kuti saali Mkristu), ayenera kugwiritsira ntchito chophimba mutu. Ndiponso, ngati, mkhalidwe wapadera, chiwalo chodzipatulira champingo chiripo pamene akuchititsa phunziro la Baibulo la panyumba lolinganizidwa pasadakhale, ayenera kuphimba mutu wake, koma mbaleyo adzayenera kupereka pemphero.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena