Mawu a M'munsi
a Mawu achiheberi amene anawamasulira kuti “Ine ndine woyamba ndi womaliza” pa Yesaya 44:6, amasonyeza kuti Yehova yekha ndiye Mulungu. Ndipo mawu achigiriki amene anawamasulira kuti “Ine ndine woyamba ndi wotsiriza” pa Chivumbulutso 1:17, amasonyeza udindo umene Yesu ali nawo.