Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Magazini a Nsanja ya Olonda, amene amafalitsidwa ndi Akhristu odzozedwa, akupitiriza kusonyeza kufunika kogwiritsira ntchito mpata umenewu mwamsanga ndi kugwira nawo mokwanira ntchito yolalikira. Mwachitsanzo, onani nkhani yakuti “Sangalalani ndi Ntchito Yopanga Ophunzira” mu Nsanja ya Olonda ya January 15, 2009, komanso yakuti “Khalani Maso” mu Nsanja ya Olonda ya March 15, 2009, ndi yakuti “Khalani ‘Achangu pa Ntchito Zabwino’” mu Nsanja ya Olonda ya June 15, 2009. Pa avereji, m’chaka cha 2010 panali anthu okwana 1,132,861 amene anachita utumiki wa upainiya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena