Mawu a M'munsi
a Pavesili, mawu akuti “aliyense wa iwo anali ndi zeze woimbira ndi mbale yagolide yodzaza ndi zofukiza,” akhoza kutanthauza akulu aja pamodzi ndi zamoyo zinayi zija. Koma nkhaniyi ikusonyeza mooneka bwino kuti mawuwa akunena za akulu 24 okha aja basi.