Mawu a M'munsi
a Kuti mumve mwatsatanetsatane nkhani ya kachisi wamkulu wauzimu, onani nkhani yakuti “Kachisi Wauzimu Wamkulu wa Yehova” mu Nsanja ya Olonda ya July 1, 1996, patsamba 14, komanso bokosi la mutu wakuti “Mmene Mzimu Woyera Unaululira Tanthauzo la Kachisi Wauzimu,” mu Nsanja ya Olonda ya July 15, 2010, patsamba 22.