Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Mawu akuti ‘phompho’ (Chigiriki, aʹbys·sos; Chiheberi, tehohmʹ) amatanthauza malo ophiphiritsa amene munthu kapena chinthu chomwe chili kumeneko sichingathe kuchita chilichonse. (Onani Chivumbulutso 9:2.) Koma mawuwa angatanthauzenso nyanja yaikulu. Mawu achiheberiwo kawirikawiri amawamasulira kuti “madzi akuya.” (Salimo 71:20; 106:9; Yona 2:5) Choncho “chilombo chotuluka muphompho” n’chimodzimodzi ndi ‘chilombo chotuluka m’nyanja.’—Chivumbulutso 11:7; 13:1.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena