Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Tikafufuza zimene zinachitikira anthu a Mulungu pa nthawiyi, zikuoneka kuti masiku atatu ndi hafu amenewa si nthawi yeniyeni ya maola 84, ngakhale kuti miyezi 42 ikuimira zaka zenizeni zitatu ndi hafu. N’kutheka kuti nthawi ya masiku atatu ndi hafu, yomwe inayamba zaka zitatu ndi hafu zitatha, yatchulidwa kawiri (pa vesi 9 ndi 11) posonyeza kuti ndi nthawi yaifupi poyerekezera ndi zaka zenizeni zitatu ndi hafu zimene mbonizo zinkagwira ntchito zili pa mavuto ambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena