Mawu a M'munsi
b Koma onani kuti lemba la Chivumbulutso 12:9 likunena za ‘chinjokacho ndi angelo ake.’ Choncho Mdyerekezi atadzipanga kukhala mulungu wonyenga, anafunanso kukhala mkulu wa angelo, koma Baibulo silimutchula ndi dzina lakuti mkulu wa angelo.