Mawu a M'munsi
a Monga mmene lemba la 1 Akorinto 4:8 likusonyezera, Akhristu odzozedwa sayamba kulamulira monga mafumu adakali padziko lapansi. Komabe, mogwirizana ndi nkhani imene ikufotokozedwa pa Chivumbulutso 14:3, 6, 12 ndi 13, iwo amaimba nawo nyimbo yatsopanoyo polalikira uthenga wabwino pamene akupirira mpaka pamapeto a moyo wawo wapadziko lapansi.