Mawu a M'munsi
b Zimenezi zikugwirizana ndi mfundo yakuti mayina achiheberi anagwiritsidwanso ntchito m’masomphenya ena. Mwachitsanzo, Yesu anapatsidwa dzina lachiheberi lakuti “Abadoni” (kutanthauza “Chiwonongeko”) ndipo adzaweruza adani ake “kumalo amene m’Chiheberi amatchedwa Haramagedo.”—Chivumbulutso 9:11; 16:16.