Mawu a M'munsi
c Lembali limati nyimboyo inali “yokhala ngati yatsopano,” chifukwa nyimboyo inalembedwa kalekale m’maulosi. Koma panalibe amene anali woyenerera kuiimba. Tsopano pamene Ufumuwo wakhazikitsidwa ndiponso pamene oyera akuukitsidwa, maulosiwo ayamba kukwaniritsidwa, ndipo ndi nthawi yoti nyimbo yosangalatsayo iimbidwe mwanthetemya.