Mawu a M'munsi
d Yerekezerani ndi mawu amene munthu wina wolemba mabuku wa ku Roma, dzina lake Seneca, anauza wansembe wamkazi yemwe ankachita uhule (mawuwa analembedwa ndi Swete m’buku lake). Iye anati: “Iwe mtsikana, unaimirira m’nyumba yochitira zauhule . . . ndipo dzina lako linkalendewera pamphumi pako. Unkapatsidwa ndalama chifukwa cha ntchito zako zochititsa manyazi.”—Controv. i, 2.