Mawu a M'munsi
b Pa November 20, 1940, mayiko a Germany, Italy, Japan ndi Hungary anasainirana pangano loti akhazikitse bungwe la League of Nations latsopano. Patapita masiku anayi akuluakulu a Katolika ku Vatican anaulutsa pawailesi mwambo wa Misa ndiponso pemphero lopempherera kuti zipembedzo zibweretse mtendere ndi dongosolo latsopano lochitira zinthu. Koma bungwe latsopano limeneli silinapite patali.