Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Chikhulupiriro chakuti pali milungu itatu mwa Mulungu mmodzi chinachokera ku Babulo wakale kumene anthu ankalambira milungu imene inkakhala itatu nthawi zonse. Milungu imeneyi inali Shamashi mulungu wa dzuwa, Sini mulungu wa mwezi ndi Ishitara mulungu wa nyenyezi. Aiguputo nawonso ankachita zomwezi polambira Osirisi, Isisi ndi Horasi. Ndipo zithunzi za Ashuri, mulungu wamkulu wa Asuri, zimasonyeza kuti anali ndi mitu itatu. Potengera zimenezi, m’matchalitchi a Katolika mumapezeka zifaniziro za Mulungu wa mitu itatu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena