Mawu a M'munsi
d Potanthauzira mawu akuti Yehova Mulungu, buku lina lotanthauzira mawu limene linasindikizidwa mu 1993 linati, Yehova Mulungu ndi “Mulungu yekhayo amene Mboni za Yehova zimalambira ndi kuvomereza kuti ndiye Mulungu woona.”—Webster’s Third New International Dictionary.