Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Malemba ena amanena kuti Yesu anali m’Manda pa nthawi imene anali wakufa. (Machitidwe 2:31) Komabe tisaganize kuti nthawi zonse tanthauzo la mawu akuti Manda limafanana ndi tanthauzo la mawu akuti phompho. Baibulo limatiuza kuti Satana komanso chilombo adzaponyedwa kuphompho. Koma limasonyeza kuti amene amapita ku Manda ndi anthu okha ndipo amagona mu imfa, kuyembekezera kudzaukitsidwa.—Yobu 14:13; Chivumbulutso 20:13.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena