Mawu a M'munsi
b Zikuoneka kuti nkhwangwa (Chigiriki peʹle·kus) ndi chida chimene chinkagwiritsidwa ntchito popha munthu ku Roma, ngakhale kuti pofika m’nthawi ya Yohane anthu ankagwiritsa ntchito kwambiri lupanga. (Machitidwe 12:2) Choncho mawu achigiriki (pe·pe·le·kis·meʹnon) amene palembali anawamasulira kuti “anaphedwa ndi nkhwangwa” akungotanthauza “kuphedwa.”