Mawu a M'munsi
a “Chisulizo chapamwamba” (kapena “njira yosuliza ya m’mbiri”) ali mawu ogwiritsiridwa ntchito kufotokoza kuphunziridwa kwa Baibulo ncholinga cha kupeza tsatanetsatane wonga ngati woliyambitsa, magwero a mawu ake, ndi nthaŵi ya kulembedwa kwa bukhu lirilonse.