Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Mokondweretsa, chifanizo cha wolamulira wakale chopezeka kumpoto kwa Siriya mu 1970 chinasonyeza kuti sikunali kwachilendo kwa wolamulira kutchedwa mfumu pamene, kwenikweni, iye anali ndi ulamuliro wocheperapo. Chifanizocho chinali cha wolamulira wa Gozan ndipo chinalembedwa mawu m’Chisuri ndi Chiaramu. Mawu olembedwa m’Chisuriwo anatcha munthuyo bwanamkubwa wa Gozan, koma mawu olembedwa m’Chiaramu ofanana nawo anamutcha mfumu.9 Chotero sikukakhala kosiyana ndi kwina kulikonse kuti Belisazara atchedwe kalonga mfumu m’zolembedwa zaukumu Zababulo pamene kuli kwakuti m’cholembedwa Chachiaramu chonena za Danieli iye akutchedwa mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena