Mawu a M'munsi
a Tikunena kuti “kaŵirikaŵiri,” chifukwa chakuti zozizwitsa zina m’Baibulo zingakhale zitaloŵetsamo zochitika zachilengedwe zonga ngati chivomezi kapena zigumukire. Komabe, izo zimawonedwabe kukhala zozizwitsa, chifukwa chakuti izo zinachitika ndendende panthaŵi imene izo zinafunidwa ndipo chotero mwachiwonekere zinali kutsogozedwa ndi Mulungu.—Yoswa 3:15, 16; 6:20.