Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ponena za ana a m’mabanja a zipembedzo zosiyana, Steven Carr Reuben, Ph.D., m’buku lake lakuti Raising Jewish Children in a Contemporary World, akuti: “Ana amasokonezeka pamene makolo amakhala ndi moyo wobisa zimene iwo ali kwenikweni, wosokoneza, wamseri, ndi wopeŵa nkhani za chipembedzo. Pamene makolo ali omasuka, oona mtima, ofotokoza bwino zikhulupiriro zawo, miyezo, ndi za mapwando awo, ana amakula ndi chisungiko ndi odzimva kukhala ofunika mumkhalidwe wa chipembedzo umene uli wofunika kwambiri pa kukula kwa chidaliro chawo ndi chidziŵitso ponena za malo awo m’dziko.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena