Mawu a M'munsi
a M’buku la malangizo opeŵera kutseguka m’mimba—nthenda yofala imene imapha makanda ambiri—World Health Organization ikuti: “Ngati mulibe chimbudzi: pitani kuthengo kutali ndi nyumba, ndi kutali ndi malo oseŵererako ana, ndi pamtunda wa mamita osachepera 10 kuchokera pamadzi; fotserani zonyansazo ndi dothi.”