Mawu a M'munsi
a Ngati Mkristu wachichepere atenga mimba yapathengo, mpingo wachikristu sumalekerera konse zimene iye wachita. Koma ngati alapa, akulu a mpingo ndi ena mumpingomo angafune kupereka thandizo.
a Ngati Mkristu wachichepere atenga mimba yapathengo, mpingo wachikristu sumalekerera konse zimene iye wachita. Koma ngati alapa, akulu a mpingo ndi ena mumpingomo angafune kupereka thandizo.