Mawu a M'munsi
a Mwachitsanzo, ngakhale openda zakuthambo amakono okonda kutenga zinthu mmene zilili amalankhula za “kutuluka” ndi “kuloŵa” kwa dzuŵa, nyenyezi, ndi magulu a nyenyezi—ngakhale kuti zimenezi, kwenikweni, zimaoneka ngati zikuyenda chifukwa cha kuzungulira kwa dziko lapansi.