Mawu a M'munsi
a Atapeza zimenezo, Profesa André Lemaire anatero kuti mzera wokonzedwanso pambuyo powonongeka wa pamwala wa Mesha (wodziŵikanso kuti Mwala wa Moabu), umene unapezeka m’chaka cha 1868, umasonyeza kuti mwalawo umatchulanso “Nyumba ya Davide.”4