Mawu a M'munsi
a Liwu lachihebri lakuti da·vaqʹ, lotembenuzidwa kuti “nadzadziphatika” panopo, “lili ndi tanthauzo la kummamatira wina wake mwachikondi ndi mokhulupirika.”4 M’Chigiriki, liwu lotembenuzidwa kuti “nadzaphatikizana” pa Mateyu 19:5 lili paubale ndi liwu lotanthauza “kumamatiza,” “kuphatika ndi sementi,” “kulumikizana zolimba.”5