Mawu a M'munsi
b M’nthaŵi za m’Baibulo, liwulo “nthyole” (Chihebri, sheʹvet) linali kutanthauza “mtengo” kapena “ndodo,” ngati ija imene mbusa amagwiritsira ntchito.10 Pano, nthyole ya ulamuliro ikutanthauza kulangiza mwachikondi, osati nkhanza yokhaulitsa ayi.—Yerekezerani ndi Salmo 23:4.