Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pali umboni wodalirika wakuti mabuku a m’Malemba Achihebri​—kuphatikizapo la Yesaya—​analembedwa kale kwambiri zisanayambe zaka za zana loyamba C.E. Wolemba mbiri Josephus (m’zaka za zana loyamba C.E.) anatero kuti mpambo wa mabuku ovomerezedwa a m’Malemba Achihebri unali utakhazikitsidwa kalekale masiku ake asanafike.8 Ndiponso, Baibulo lachigiriki la Septuagint, matembenuzidwe a Malemba Achihebri m’Chigiriki, linayambidwa m’zaka za zana lachitatu B.C.E. ndipo linamalizidwa podzafika zaka za zana lachiŵiri B.C.E.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena