Mawu a M'munsi
b Ngati mukufuna malongosoledwe ena a maulosi a Baibulo ndi umboni wake wa m’mbiri yakale wakuti anakwaniritsidwa, chonde onani buku lakuti Baibulo—Kodi Ndilo Mawu a Mulungu Kapena a Munthu?, lofalitsidwa ndi Watchtower Bible and Tract Society of New York, Inc., masamba 117-33.