Mawu a M'munsi
d Magazini yotchedwa Biblical Archaeology Review inati: “Akatswiri a Babulo anaika m’magulu osiyanasiyana zikwizikwi za zizindikiro za malaulo. . . . Pamene Belisazara analamula kuti auzidwe tanthauzo la mawu olembedwa pakhomawo, amuna anzeru a Babulo, mosakayikira, anakafufuza m’mabuku ameneŵa a malaulo. Koma anapezeka kukhala opanda pake.”