Mawu a M'munsi
e Olemba madikishonale anena kuti liwu limene linatembenuzidwa kuti “anathedwa nzeru” limatanthauza chipwirikiti chadzaoneni, monga kuti paphwandopo panabuka chisokonezo chachikulu.
e Olemba madikishonale anena kuti liwu limene linatembenuzidwa kuti “anathedwa nzeru” limatanthauza chipwirikiti chadzaoneni, monga kuti paphwandopo panabuka chisokonezo chachikulu.