Mawu a M'munsi
a Zolemba zamakedzana zimapereka umboni wosonyeza kuti “dzenje la mikango” linalipodi m’Babulo, ponena kuti olamulira a Kum’maŵa nthaŵi zambiri ankakhala ndi malo osungiramo nyama zakuthengo.
a Zolemba zamakedzana zimapereka umboni wosonyeza kuti “dzenje la mikango” linalipodi m’Babulo, ponena kuti olamulira a Kum’maŵa nthaŵi zambiri ankakhala ndi malo osungiramo nyama zakuthengo.