Mawu a M'munsi
a Maulamuliro asanu ndi aŵiri amphamvu padziko lonse okhala ndi tanthauzo lapadera m’Baibulo ndiwo Igupto, Asiriya, Babulo, Mediya ndi Perisiya, Girisi, Roma, ndi mgwirizano wa Britain ndi America. Onseŵa n’ngofunika mwapadera chifukwa achita zinthu zokhudza anthu a Yehova.